Back to stories list

Nkhuku ndi Bongololo Chicken and Millipede Inkoko ne Ciyongoli

Written by Winny Asara

Illustrated by Magriet Brink

Translated by Sitwe Benson Mkandawire, David Mwanza

Read by Christine Mwanza

Language Nyanja

Level Level 3

Narrate full story The audio for this story is currently not available.


Nkhuku ndi Bongololo anali abwenzi. Koma anali kukonda kupikisana paiwo okha. Tsiku lina, anaganiza kusewera m’pira wa myendo kuti aone ngati katswiri ndani.

Chicken and Millipede were friends. But they were always competing with each other. One day they decided to play football to see who the best player was.

Inkoko ne Ciyongoli fyali fibusa. Nomba lyonse baaleecimfyanya. Ubushiku bumo, baatontonkenye ukuti bateye umupila pakuti bamone uwaishibishe ukuteya.


Anayenda kubwalo la m’pira ndipo anayamba masewera awo. Nkhuku inafulumira, koma Bongololo anafulumira kopambana. Nkhuku inapandira kutali koma bongololo anapandira kutali mopambana. Nkhuku inayamba kukalipa.

They went to the football field and started their game. Chicken was fast, but Millipede was faster. Chicken kicked far, but Millipede kicked further. Chicken started to feel grumpy.

Baile ku cibansa ca mupila no kwamba ukuteya. Inkoko yali iyayangukilwa nomba Iciyongoli calyangukishe ukucilapo. Inkoko yapantiile ukutali nomba Iciyongoli capantiile ukutali ukucilapo. Inkoko epakwamba ukumfwa ububi.


Anagaza kuti asewere mapenoti. Bongololo anayambira kukhala wogwira m’pira. Nkhuku inamwesa cigoli cimodzi. Tsopano inali nthawi yankhuku kuti igwire m’pira.

They decided to play a penalty shoot-out. First Millipede was goal keeper. Chicken scored only one goal. Then it was the chicken’s turn to defend the goal.

Baumfwene ukuti kube ukupantafye iyakwingisha mu cipanda. Iciyongoli ecabalilepo ukwikata mu cipanda. Inkoko yaingishafye kamo. Epakucinjana pakuti Inkoko nayo yaba mukwikata mu cipanda.


Bongololo anasewera ndipo anamwetsa. Bongololo ananyunya ndi kumwetsa. Bongololo anamwesanso ndi mutu. Bongololo anamwetsa zigoli zisanu.

Millipede kicked the ball and scored. Millipede dribbled the ball and scored. Millipede headed the ball and scored. Millipede scored five goals.

Iciyongoli epakupanta no kwingisha. Iciyongoli cabela no kwingisha. Iciyongoli cauma iyakumutwe no kwingisha. Iciyongoli caingisha utukato tusaano.


Nkhuka inakalipa kuti inagonja. Inagonja kothelathu. Bongololo anayamba kuseka cifukwa ca madandaulo amnzake pambuyo pakugonja.

Chicken was furious that she lost. She was a very bad loser. Millipede started laughing because his friend was making such a fuss.

Inkoko yalifulilwe ukuti yaluusa umupila. Iciyongoli caatampile ukuseka umunankwe pantu aaleilishanya.


Nkhuku inakalipa kwambiri ndikutsegula kamwa nameza bongololo.

Chicken was so angry that she opened her beak wide and swallowed the millipede.

Inkoko yalifulilwe saana yasoba iciyongoli no kucilya.


Pamene nkhuku inali kuyenda kunyumba, inakumana ndi amake abongololo. Amake Bongololo anafunsa nati, “Kodi wamuonako mwana wanga?” Nkhuku siyinalankhule ciriconse. Amake Bongololo anada nkhawa.

As Chicken was walking home, she met Mother Millipede. Mother Millipede asked, “Have you seen my child?” Chicken didn’t say anything. Mother Millipede was worried.

Cilya inkoko ileeya ku ŋanda, yakumanya nyina wa ciyongoli. Nyina waciyongoli eipusha ati, “Bushe naumonako umwana wandi?” Inkoko tayayaswike nangu cimo. Nyina wa ciyongoli tepakusakamana.


Amake Bongololo anamva timau tating’ono. “Ndithandizeni amai!” liu linalira. Amake Bongololo anayangana uku ndi uku, ndi kumvetsetsa ndi cidwi. Mau anacokera mumimba mwa nkhuku.

Then Mother Millipede heard a tiny voice. “Help me mom!” cried the voice. Mother Millipede looked around and listened carefully. The voice came from inside the chicken.

Elyo nyina wa ciyongoli aumfwile akalishiwi akanoono. “Mutuule maayo!” Nyina wa ciyongoli aloleeshalolesha no kumfwikisha. Ishiwi lyaleefuma mu mala ya nkoko.


Amake Bongololo anafuula nati, “Sewenzetsa mphamvu zako zapadela mwana wanga!” Bongololo atha kununkha ndi kusamveka bwino. Nkhuku inayamba kumvela bwino mthupi.

Mother Millipede shouted, “Use your special power my child!” Millipedes can make a bad smell and a terrible taste. Chicken began to feel ill.

Nyina wa ciyongoli epakupunda ati, “Bomfya amaka yobe mwana wandi!” Iciyongoli limo cilanunka ububi saana, no kumfwika ububi mu kanwa. Inkoko epakwamba ukumfwa ububi.


Nkhuku inageya. Ndipo inamela ndi kutaya mata. Ndipo inakosomola. Bongololo anali kunyansisa.

Chicken burped. Then she swallowed and spat. Then she sneezed and coughed. And coughed. The millipede was disgusting!

Inkoko yalibyolele. Yamina amate kabili yafwisa. Elyo yatesula no kukoola. Yakoola kabili. Iciyongoli tepabubi.


Nkhuku inakosomola kufikira itakosomolela panja Bongololo amene anali mumimba mwake. Bongololo ndi amai ake anakalawa ndi kukwera m’mtengo kubisala.

Chicken coughed until she coughed out the millipede that was in her stomach. Mother Millipede and her child crawled up a tree to hide.

Inkoko yakoola mpaka yakoola Iciyongoli icali mu mala. Nyina wa ciyongoli no mwana wakwe efyo baninine ku cimuti eko babelama.


Kucokera pamenepo, Bongololo ndi Nkhuku anakhala adani.

From that time, chickens and millipedes were enemies.

Ukufuma apopene inkoko ne fiyongoli fyalipatana.


Written by: Winny Asara
Illustrated by: Magriet Brink
Translated by: Sitwe Benson Mkandawire, David Mwanza
Read by: Christine Mwanza
Language: Nyanja
Level: Level 3
Source: Chicken and Millipede from African Storybook
Creative Commons License
This work is licensed under a Creative Commons Attribution 3.0 International License.
Options
Back to stories list Download PDF